Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 5:6 - Buku Lopatulika

Ndipo Seti anakhala ndi moyo zaka zana kudza zisanu, nabala Enosi;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Seti anakhala ndi moyo zaka zana kudza zisanu, nabala Enosi;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Seti ali wa zaka 105, adabereka mwana dzina lake Enosi,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pamene Seti anali ndi zaka 105, anabereka Enosi.

Onani mutuwo



Genesis 5:6
5 Mawu Ofanana  

Ndipo Adamu anadziwanso mkazi wake; ndipo anabala mwana wamwamuna, namutcha dzina lake Seti, chifukwa anati iye, Mulungu wandilowezera ine mbeu ina m'malo mwa Abele amene Kaini anamupha.


Ndiponso kwa Seti, kwa iye kunabadwa mwana wamwamuna: anamutcha dzina lake Enosi: pomwepo anthu anayamba kutchula dzina la Yehova.


Masiku ake onse anakhala ndi moyo Adamu anali zaka mazana asanu ndi anai, kudza makumi atatu; ndipo anamwalira.


ndipo Seti anakhala ndi moyo, atabala Enosi, zaka mazana asanu ndi atatu kudza zisanu ndi ziwiri: ndipo anabala ana aamuna ndi aakazi:


mwana wa Enosi, mwana wa Seti, mwana wa Adamu, mwana wa Mulungu.