Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 5:7 - Buku Lopatulika

7 ndipo Seti anakhala ndi moyo, atabala Enosi, zaka mazana asanu ndi atatu kudza zisanu ndi ziwiri: ndipo anabala ana aamuna ndi aakazi:

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 ndipo Seti anakhala ndi moyo, atabala Enosi, zaka mazana asanu ndi atatu kudza zisanu ndi ziwiri: ndipo anabala ana aamuna ndi aakazi:

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 ndipo adakhalanso ndi moyo zaka zina 807. Adaberekanso ana ena aamuna ndi aakazi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 Atabadwa Enosi, Seti anakhala ndi moyo zaka zina 807 ndipo anabereka ana ena aamuna ndi aakazi.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 5:7
4 Mawu Ofanana  

Masiku ake Adamu atabala Seti, anali zaka mazana asanu ndi atatu; ndipo anabala ana aamuna ndi aakazi.


Ndipo Seti anakhala ndi moyo zaka zana kudza zisanu, nabala Enosi;


masiku ake onse a Seti anali zaka mazana asanu ndi anai kudza khumi ndi ziwiri; ndipo anamwalira.


mwana wa Enosi, mwana wa Seti, mwana wa Adamu, mwana wa Mulungu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa