Genesis 5:6 - Buku Lopatulika6 Ndipo Seti anakhala ndi moyo zaka zana kudza zisanu, nabala Enosi; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ndipo Seti anakhala ndi moyo zaka zana kudza zisanu, nabala Enosi; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Seti ali wa zaka 105, adabereka mwana dzina lake Enosi, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Pamene Seti anali ndi zaka 105, anabereka Enosi. Onani mutuwo |