Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 4:25 - Buku Lopatulika

25 Ndipo Adamu anadziwanso mkazi wake; ndipo anabala mwana wamwamuna, namutcha dzina lake Seti, chifukwa anati iye, Mulungu wandilowezera ine mbeu ina m'malo mwa Abele amene Kaini anamupha.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

25 Ndipo Adamu anadziwanso mkazi wake; ndipo anabala mwana wamwamuna, namutcha dzina lake Seti: Chifukwa, nati iye, Mulungu wandilowezera ine mbeu ina m'malo mwa Abele amene Kaini anamupha.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

25 Adamu adakhalanso ndi Heva mkazi wake, ndipo adatenga pathupi nabala mwana. Tsono Hevayo adati, “Mulungu wandipatsa mwana woloŵa m'malo mwa Abele uja amene adaphedwa ndi Kaini.” Mwanayo adamutcha Seti.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

25 Adamu anagonanso malo amodzi ndi mkazi wake, ndipo anabereka mwana wamwamuna namutcha Seti, kutanthauza kuti, “Mulungu wandipatsa mwana wina mʼmalo mwa Abele, popeza Kaini anamupha.”

Onani mutuwo Koperani




Genesis 4:25
7 Mawu Ofanana  

Kaini ndipo ananena ndi Abele mphwake. Ndipo panali pamene anali kumunda, Kaini anamuukira Abele mphwake, namupha.


Ndipo Seti anakhala ndi moyo zaka zana kudza zisanu, nabala Enosi;


Adamu, Seti, Enosi,


mwana wa Enosi, mwana wa Seti, mwana wa Adamu, mwana wa Mulungu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa