Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 3:38 - Buku Lopatulika

38 mwana wa Enosi, mwana wa Seti, mwana wa Adamu, mwana wa Mulungu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

38 mwana wa Enosi, mwana wa Seti, mwana wa Adamu, mwana wa Mulungu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

38 mwana wa Enosi, mwana wa Seti, mwana wa Adamu, amene anali mwana wa Mulungu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

38 mwana wa Enosi, mwana wa Seti, mwana wa Adamu, mwana wa Mulungu.

Onani mutuwo Koperani




Luka 3:38
11 Mawu Ofanana  

Ndipo Yehova Mulungu anaumba munthu ndi dothi lapansi, nauzira mpweya wa moyo m'mphuno mwake; munthuyo nakhala wamoyo.


Ndipo Adamu anadziwanso mkazi wake; ndipo anabala mwana wamwamuna, namutcha dzina lake Seti, chifukwa anati iye, Mulungu wandilowezera ine mbeu ina m'malo mwa Abele amene Kaini anamupha.


Ndiponso kwa Seti, kwa iye kunabadwa mwana wamwamuna: anamutcha dzina lake Enosi: pomwepo anthu anayamba kutchula dzina la Yehova.


Koma tsopano, Yehova, Inu ndinu Atate wathu; ife tili dongo, ndipo Inu ndinu Muumbi wathu; ndipo ife tonse tili ntchito ya dzanja lanu.


mwana wa Metusela, mwana wa Enoki, mwana wa Yaredi, mwana wa Mahalalele, mwana wa Kainani,


Ndipo Yesu, wodzala ndi Mzimu Woyera, anabwera kuchokera ku Yordani, natsogozedwa ndi Mzimu kunka kuchipululu


Koteronso kwalembedwa, Munthu woyamba, Adamu, anakhala mzimu wamoyo. Adamu wotsirizayo anakhala mzimu wakulenga moyo.


Munthu woyambayo ali wapansi, wanthaka. Munthu wachiwiri ali wakumwamba.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa