Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 42:8 - Buku Lopatulika

Ndipo Yosefe anazindikira abale ake, koma iwo sanamzindikire iye.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Yosefe anazindikira abale ake, koma iwo sanamzindikire iye.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Yosefe adaŵazindikira abale ake aja, koma iwo sadamzindikire.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ngakhale Yosefe anawazindikira abale ake, koma iwo sanamuzindikire.

Onani mutuwo



Genesis 42:8
5 Mawu Ofanana  

Mibadwo ya Yakobo ndi iyi; Yosefe anali wa zaka khumi ndi zisanu ndi ziwiri analinkudyetsa zoweta pamodzi ndi abale ake; ndipo anali mnyamata pamodzi ndi ana a Biliha, ndi ana aamuna a Zilipa, akazi a atate wake; ndipo Yosefe anamfotokozera atate wake mbiri yao yoipa.


Ndipo Yosefe anali wa zaka makumi atatu pamene iye anaima pamaso pa Farao mfumu ya Aejipito. Ndipo Yosefe anatuluka pamaso pa Farao, napitapita padziko lonse la Ejipito.


Koma maso ao anagwidwa kuti asamzindikire Iye.


M'mene adanena izi, anacheuka m'mbuyo, naona Yesu ali chilili, ndipo sanadziwe kuti ndiye Yesu.


Koma pakuyamba kucha, Yesu anaimirira pambali pa nyanja, komatu ophunzirawo sanadziwe kuti ndiye Yesu.