Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 21:4 - Buku Lopatulika

4 Koma pakuyamba kucha, Yesu anaimirira pambali pa nyanja, komatu ophunzirawo sanadziwe kuti ndiye Yesu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Koma pakuyamba kucha, Yesu anaimirira pambali pa nyanja, komatu ophunzirawo sanadziwa kuti ndiye Yesu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Kutacha Yesu adaimirira pa mtunda. Komabe ophunzira aja sadazindikire kuti ndi Yesu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Mmamawa, Yesu anayimirira mʼmbali mwa nyanja, koma ophunzira ake sanazindikire kuti anali Yesu.

Onani mutuwo Koperani




Yohane 21:4
5 Mawu Ofanana  

Ndipo Yosefe anazindikira abale ake, koma iwo sanamzindikire iye.


Ndipo zitatha izi, anaonekanso Iye m'maonekedwe ena kwa awiri a iwo alikuyenda kupita kumidzi.


Ndipo maso ao anatseguka, ndipo anamzindikira Iye; ndipo anawakanganukira Iye, nawachokera.


M'mene adanena izi, anacheuka m'mbuyo, naona Yesu ali chilili, ndipo sanadziwe kuti ndiye Yesu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa