Yohane 21:5 - Buku Lopatulika5 Yesu ananena nao, Ananu, muli nako kanthu kakudya kodi? Anamyankha Iye, Iai. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Yesu ananena nao, Ananu, muli nako kanthu kakudya kodi? Anamyankha Iye, Iai. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Tsono Iye adaŵafunsa kuti, “Kodi anzathu, mwaphako kanthu ngati?” Iwo adati, “Ai ndithu, tabwera chabe.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Yesu anawafunsa iwo kuti, “Anzanga, kodi muli nsomba?” Iwo anayankha kuti, “Ayi.” Onani mutuwo |