Yohane 20:14 - Buku Lopatulika14 M'mene adanena izi, anacheuka m'mbuyo, naona Yesu ali chilili, ndipo sanadziwe kuti ndiye Yesu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 M'mene adanena izi, anacheuka m'mbuyo, naona Yesu ali chilili, ndipo sanadziwa kuti ndiye Yesu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Atanena zimenezi adacheuka, naona Yesu ataimirira pomwepo, koma sadamzindikire kuti ndi Yesu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Atanena izi, iye anatembenuka ndipo anaona Yesu atayima potero koma iye sanazindikire kuti anali Yesu. Onani mutuwo |