Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 32:1 - Buku Lopatulika

Ndipo Yakobo anankabe ulendo wake, ndipo amithenga a Mulungu anakomana naye.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Yakobo anankabe ulendo wake, ndipo amithenga a Mulungu anakomana naye.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Yakobe adanyamuka ulendo wake, ndipo angelo a Mulungu adakumana naye.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Nayenso Yakobo analowera njira yake, ndipo angelo a Mulungu anakumana naye.

Onani mutuwo



Genesis 32:1
9 Mawu Ofanana  

Ndipo Yehova anapita atatha kunena naye Abrahamu: ndipo Abrahamu anabwera kumalo kwake.


Ndipo anamdalitsa Rebeka, nati kwa iye, Mlongo wathu ndiwe, iwe ukhale amai wa anthu zikwizikwi, mbeu zako zigonjetse chipata cha iwo akudana nao.


Ndipo sunandiloleze ine ndimpsompsone ana anga aamuna ndi aakazi? Wapusa iwe pakuchita chotero.


Mngelo wa Yehova azinga kuwatchinjiriza iwo akuopa Iye, nawalanditsa iwo.


Pakuti adzalamulira angelo ake za iwe, akusunge m'njira zako zonse.


ngati Paulo, kapena Apolo, kapena Kefa, kapena dziko lapansi, kapena moyo, kapena imfa, kapena za makono ano, kapena zilinkudza; zonse ndi zanu;


kuti mu Mpingo azindikiritse tsopano kwa akulu ndi maulamuliro m'zakumwamba nzeru ya mitundumitundu ya Mulungu,


atakhala wakuposa angelo, monga momwe adalowa dzina lakuposa iwo.