Masalimo 91:11 - Buku Lopatulika11 Pakuti adzalamulira angelo ake za iwe, akusunge m'njira zako zonse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Pakuti adzalamulira angelo ake za iwe, akusunge m'njira zako zonse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Chauta adzapatsa angelo ake ntchito yoti azikulonda kulikonse kumene upite. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Pakuti adzalamulira angelo ake za iwe, kuti akutchinjirize mosamala pa njira zako zonse; Onani mutuwo |