Genesis 18:33 - Buku Lopatulika33 Ndipo Yehova anapita atatha kunena naye Abrahamu: ndipo Abrahamu anabwera kumalo kwake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201433 Ndipo Yehova anapita atatha kunena naye Abrahamu: ndipo Abrahamu anabwera kumalo kwake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa33 Chauta atatha kulankhula ndi Abrahamu, adachokapo, Abrahamuyo nkumabwerera kwao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero33 Yehova atatsiriza kuyankhula ndi Abrahamu, anachoka ndipo Abrahamu anabwerera ku nyumba yake. Onani mutuwo |