Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 3:9 - Buku Lopatulika

Ndipo Yehova Mulungu anaitana mwamunayo nati kwa iye, Uli kuti?

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Yehova Mulungu anaitana mwamunayo nati kwa iye, Uli kuti?

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Koma Chauta adamuitana Adamu uja kuti, “Kodi uli kuti?”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Yehova Mulungu anayitana munthu uja kuti, “Uli kuti?”

Onani mutuwo



Genesis 3:9
8 Mawu Ofanana  

Ndipo Yehova anatsikira kudzaona mzinda ndi nsanja imene analinkumanga ana a anthu.


Ndipo anati, Hagara, mdzakazi wake wa Sarai, ufumira kuti? Unka kuti? Ndipo anati, Ndithawa ine kumaso kwake kwa wakuka wanga Sarai.


Ndipo anati kwa iye, Ali kuti Sara mkazi wako? Ndipo anati, Taonani m'hemamo.


Yehova ndipo anati kwa Kaini, Ali kuti Abele mphwako? Ndipo anati, Sindidziwai: kodi ndine woyang'anira mphwanga?


Pamenepo analowa, naima kwa mbuye wake. Ndipo Elisa ananena naye, Ufuma kuti Gehazi? Nati, Ngati mnyamata wanu wayenda konse?