Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Genesis 3:9 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Yehova Mulungu anayitana munthu uja kuti, “Uli kuti?”

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

9 Ndipo Yehova Mulungu anaitana mwamunayo nati kwa iye, Uli kuti?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Ndipo Yehova Mulungu anaitana mwamunayo nati kwa iye, Uli kuti?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Koma Chauta adamuitana Adamu uja kuti, “Kodi uli kuti?”

Onani mutuwo Koperani




Genesis 3:9
8 Mawu Ofanana  

Koma Yehova anatsika kudzaona mzindawo ndi nsanja imene anthu aja ankayimanga.


Ndipo mngeloyo anati, “Hagara, iwe wantchito wa Sarai, ukuchokera kuti ndipo ukupita kuti?” Iye anayankha, “Ndikuthawa mbuye wanga Sarai.”


Anthuwo anafunsa Abrahamu kuti, “Mkazi wako Sara ali kuti?” Iye anati, “Ali mu tentimu.”


Ndipo Yehova anamufunsa Kaini kuti, “Ali kuti mʼbale wako Abele?” Iye anayankha kuti, “Sindikudziwa. Kodi ine ndine wosunga mʼbale wanga?”


Kenaka analowa mʼnyumbamo nakayima pamaso pa mbuye wake Elisa. Elisa anafunsa kuti, “Kodi Gehazi unali kuti?” Iye anayankha kuti, “Mtumiki wanu sanapite kwina kulikonse.”


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa