Genesis 3:10 - Buku Lopatulika10 Ndipo anati, Ndinamva mau anu m'mundamu, ndipo ndinaopa chifukwa ndinali wamaliseche ine; ndipo ndinabisala. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ndipo anati, Ndinamva mau anu m'mundamu, ndipo ndinaopa chifukwa ndinali wamaliseche ine; ndipo ndinabisala. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Adamu adayankha kuti, “Ndinakumvani m'mundamu ndipo ndinaopa, ndiye ndinabisala ntaona kuti ndili maliseche.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Iye anayankha, “Ndinakumvani mʼmundamo, ndipo ndimaopa chifukwa ndinali maliseche; choncho ndinabisala.” Onani mutuwo |