Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 3:9 - Buku Lopatulika

9 Ndipo Yehova Mulungu anaitana mwamunayo nati kwa iye, Uli kuti?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Ndipo Yehova Mulungu anaitana mwamunayo nati kwa iye, Uli kuti?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Koma Chauta adamuitana Adamu uja kuti, “Kodi uli kuti?”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Yehova Mulungu anayitana munthu uja kuti, “Uli kuti?”

Onani mutuwo Koperani




Genesis 3:9
8 Mawu Ofanana  

Ndipo Yehova anatsikira kudzaona mzinda ndi nsanja imene analinkumanga ana a anthu.


Ndipo anati, Hagara, mdzakazi wake wa Sarai, ufumira kuti? Unka kuti? Ndipo anati, Ndithawa ine kumaso kwake kwa wakuka wanga Sarai.


Ndipo anati kwa iye, Ali kuti Sara mkazi wako? Ndipo anati, Taonani m'hemamo.


Yehova ndipo anati kwa Kaini, Ali kuti Abele mphwako? Ndipo anati, Sindidziwai: kodi ndine woyang'anira mphwanga?


Pamenepo analowa, naima kwa mbuye wake. Ndipo Elisa ananena naye, Ufuma kuti Gehazi? Nati, Ngati mnyamata wanu wayenda konse?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa