Genesis 3:9 - Buku Lopatulika9 Ndipo Yehova Mulungu anaitana mwamunayo nati kwa iye, Uli kuti? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndipo Yehova Mulungu anaitana mwamunayo nati kwa iye, Uli kuti? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Koma Chauta adamuitana Adamu uja kuti, “Kodi uli kuti?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Yehova Mulungu anayitana munthu uja kuti, “Uli kuti?” Onani mutuwo |