Genesis 11:5 - Buku Lopatulika5 Ndipo Yehova anatsikira kudzaona mzinda ndi nsanja imene analinkumanga ana a anthu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ndipo Yehova anatsikira kudzaona mudzi ndi nsanja imene analinkumanga ana a anthu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Tsono Chauta adatsika kudzaona mzindawo, pamodzi ndi nsanja imene anthu ankamanga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Koma Yehova anatsika kudzaona mzindawo ndi nsanja imene anthu aja ankayimanga. Onani mutuwo |