Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 26:23 - Buku Lopatulika

Ndipo anachoka kumeneko nakwera kunka ku Beereseba.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anachoka kumeneko nakwera kunka ku Beereseba.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Patapita nthaŵi, Isaki adachoka napita ku Beereseba.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Kenaka Isake anachoka ku malo kuja kupita ku Beeriseba.

Onani mutuwo



Genesis 26:23
7 Mawu Ofanana  

Ndipo Abrahamu analawira m'mamawa, natenga mkate ndi thumba la madzi, nampatsa Hagara, naika paphewa pake, ndi mwana, namchotsa iye: ndipo iye anamuka, nasocherera m'chipululu cha Beereseba.


Chifukwa chake anatcha malowo Beereseba: chifukwa pamenepo analumbira onse awiri.


Ndipo Abrahamu anabwera kwa anyamata ake, ndipo anauka nayenda pamodzi kumuka ku Beereseba; ndipo anakhala Abrahamu pa Beereseba.


Ndipo Yakobo anachoka mu Beereseba, nanka ku Harani.


Ndipo Israele anamuka ulendo wake ndi zonse anali nazo, nafika ku Beereseba, napereka nsembe kwa Mulungu wa Isaki atate wake.


koma musamafuna Betele, kapena kumalowa mu Giligala; musamapita ku Beereseba; pakuti Giligala adzalowadi m'ndende, ndi Betele adzasanduka chabe.


Pamenepo anatuluka ana onse a Israele, nuunjikana msonkhano kwa Yehova ku Mizipa ngati munthu mmodzi, kuyambira ku Dani mpaka Beereseba ndi dziko la Giliyadi lomwe.