Genesis 28:10 - Buku Lopatulika10 Ndipo Yakobo anachoka mu Beereseba, nanka ku Harani. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ndipo Yakobo anachoka m'Beereseba, nanka ku Harani. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Yakobe adanyamuka ulendo kuchoka ku Beereseba, kupita ku Harani. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Yakobo ananyamuka pa ulendo kuchoka ku Beeriseba kupita ku Harani. Onani mutuwo |