Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 16:9 - Buku Lopatulika

Ndipo mthenga wa Yehova anati kwa iye, Bwera kwa wakuka wako, udzichepetse wekha pamanja pake.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo mthenga wa Yehova anati kwa iye, Bwera kwa wakuka wako, udzichepetse wekha pamanja pake.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mngelo wa Chautayo adati, “Iyai, bwerera kwa Sarai, ukamgonjere.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mngelo wa Yehova anamuwuza kuti, “Bwerera kwa mbuye wako ndipo ukamugonjere.

Onani mutuwo



Genesis 16:9
9 Mawu Ofanana  

Ndipo mthenga wa Yehova anati kwa iye, Ndidzachulukitsa ndithu mbeu zako, kuti unyinji wao sudzawerengeka.


Koma Abramu anati kwa Sarai, Taona, mdzakazi wako ali m'dzanja lako, umchitire iye chimene chikukomera m'maso mwako. Ndipo Sarai anamsautsa iye, ndipo anathawa kumaso kwake.


Ndipo anati, Hagara, mdzakazi wake wa Sarai, ufumira kuti? Unka kuti? Ndipo anati, Ndithawa ine kumaso kwake kwa wakuka wanga Sarai.


Ngati mkulu akukwiyira, usasiye malo ako; chifukwa chifatso chipembedza utachimwa kwambiri.


ndi kumverana wina ndi mnzake m'kuopa Khristu.


Akapolo amvere ambuye ao a iwo okha, nawakondweretse m'zonse; osakana mau ao;