Aefeso 5:21 - Buku Lopatulika21 ndi kumverana wina ndi mnzake m'kuopa Khristu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 ndi kumverana wina ndi mnzake m'kuopa Khristu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Inu amene mumaopa Khristu, muzimverana. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Gonjeranani wina ndi mnzake, kuonetsa kuopa Khristu. Onani mutuwo |