Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Aefeso 5:22 - Buku Lopatulika

22 Akazi inu, mverani amuna anu a inu eni, monga kumvera Ambuye.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

22 Akazi inu, mverani amuna anu a inu eni, monga kumvera Ambuye.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

22 Inu akazi, muzimvera amuna anu, monga mumamvera Ambuye.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

22 Inu akazi, muzigonjera amuna anu, monga mumagonjera kwa Ambuye.

Onani mutuwo Koperani




Aefeso 5:22
14 Mawu Ofanana  

Kwa mkaziyo ndipo anati, Ndidzachulukitsa kusauka kwako ndi potenga mimba pako; udzasauka pakubala: udzakhumba mwamuna wako, ndipo iye adzakulamulira iwe.


Ndipo mau amene adzaika mfumu akamveka mu ufumu wake wonse, (pakuti ndiwo waukulu), akazi onse adzachitira amuna ao ulemu, aakulu ndi aang'ono.


natumiza makalata kumaiko onse a mfumu, kudziko lililonse monga mwa chilembedwe chao, ndi kumtundu uliwonse monga mwa chinenedwe chao, kuti mwamuna aliyense akhale wamkulu m'nyumba yakeyake, nawabukitse monga mwa chinenedwe cha anthu a mtundu wake.


Akazi akhale chete mu Mipingo. Pakuti sikuloledwa kwa iwo kulankhula. Koma akhale omvera, monganso chilamulo chinena.


Akazi inu, mverani amuna anu a inu eni, monga kumvera Ambuye.


Akapolo inu, mverani iwo amene ali ambuye anu monga mwa thupi, ndi kuwaopa ndi kunthunthumira nao, ndi mtima wanu wosakumbukira kanthu kena, monga kwa Khristu;


Chifukwa chake ngati munaukitsidwa pamodzi ndi Khristu, funani zakumwamba, kumene kuli Khristu wokhala padzanja lamanja la Mulungu.


Akazi inu, muzimvera amuna anu, monga kuyenera mwa Ambuye.


akhale odziletsa, odekha, ochita m'nyumba mwao, okoma, akumvera amuna a iwo okha, kuti mau a Mulungu angachitidwe mwano.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa