Aefeso 5:20 - Buku Lopatulika20 ndi kuyamika Mulungu Atate masiku onse, chifukwa cha zonse, m'dzina la Ambuye wathu Yesu Khristu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 ndi kuyamika Mulungu Atate masiku onse, chifukwa cha zonse, m'dzina la Ambuye wathu Yesu Khristu; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Muziyamika Mulungu Atate nthaŵi zonse chifukwa cha zonse, m'dzina la Ambuye athu Yesu Khristu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Muziyamika Mulungu Atate nthawi zonse chifukwa cha zonse, mʼdzina la Ambuye athu Yesu Khristu. Onani mutuwo |