Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Tito 2:9 - Buku Lopatulika

9 Akapolo amvere ambuye ao a iwo okha, nawakondweretse m'zonse; osakana mau ao;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Akapolo amvere ambuye ao a iwo okha, nawakondweretse m'zonse; osakana mau ao;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Antchito azimvera ambuye ao, aziŵakondweretsa pa zonse. Asamatsutsana nawo

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Phunzitsa akapolo kuti azigonjera ambuye awo mu zinthu zonse ndi kuwakondweretsa. Asamatsutsane nawo

Onani mutuwo Koperani




Tito 2:9
5 Mawu Ofanana  

Komatu monga Mpingo amvera Khristu, koteronso akazi amvere amuna ao m'zinthu zonse.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa