Tito 2:8 - Buku Lopatulika8 mau olama osatsutsika; kuti iye wakutsutsana achite manyazi, posakhala nako kanthu koipa kakutinenera ife. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 mau olama osatsutsika; kuti iye wakutsutsana achite manyazi, posakhala nako kanthu koipa kakutinenera ife. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Mau ako akhale oona, kuti anthu asadzathe kuŵatsutsa. Motero wotsutsana nawe adzachita manyazi, atasoŵa kalikonse koipa kuti atinenere. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Phunzitsa choonadi kuti anthu asapeze chokutsutsa, motero wotsutsana nawe adzachita manyazi chifukwa adzasowa kanthu koyipa kuti atinenere. Onani mutuwo |