Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 34:8 - Buku Lopatulika

Ndipo Mose anafulumira, naweramira pansi nalambira.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Mose anafulumira, naweramira pansi nalambira.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pamenepo Mose adagwada pansi napembedza.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pamenepo Mose anawerama pansi napembedza.

Onani mutuwo



Eksodo 34:8
5 Mawu Ofanana  

Ndipo Abramu anagwa nkhope pansi, ndipo Mulungu ananena naye kuti,


Ndipo Yosefe anatulutsa iwo pakati pa maondo ake, nawerama ndi nkhope yake pansi.


Ndipo Yehosafati anawerama mutu wake, nkhope yake pansi; ndi Ayuda onse, ndi okhala mu Yerusalemu anagwa pansi pamaso pa Yehova, nalambira Yehova.


Ndipo anthuwo anakhulupirira; ndipo pamene anamva kuti Yehova adawazonda ana a Israele, ndi kuti adaona mazunzo ao, anawerama, nalambira Mulungu.


monga momwe ndinapangana nanu muja munatuluka mu Ejipito, ndi Mzimu wanga unakhala pakati pa inu; musamaopa inu.