Genesis 17:3 - Buku Lopatulika3 Ndipo Abramu anagwa nkhope pansi, ndipo Mulungu ananena naye kuti, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndipo Abramu anagwa nkhope pansi, ndipo Yehova ananena naye kuti, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Pomwepo Abramu adagwada pansi ndipo Mulungu adati, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Pomwepo Abramu anadziponya pansi ndipo Mulungu anati kwa iye, Onani mutuwo |