Genesis 17:4 - Buku Lopatulika4 Koma Ine, taona, pangano langa lili ndi iwe, ndipo udzakhala iwe atate wa khamu la mitundu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Koma Ine, taona, pangano langa lili ndi iwe, ndipo udzakhala iwe atate wa khamu la mitundu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 “Nachi chipangano chimene ndidzachite nawe. Ndikulonjeza kuti udzakhala kholo la anthu a mitundu yambiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 “Pangano langa ndi iwe ndi ili: Udzakhala kholo la mitundu yambiri ya anthu. Onani mutuwo |