Genesis 17:2 - Buku Lopatulika2 Ndipo ndidzapangana pangano langa ndi Ine ndi iwe, ndipo ndidzachulukitsa iwe kwambiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndipo ndidzapangana pangano langa ndi Ine ndi iwe, ndipo ndidzachulukitsa iwe kwambiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Ndidzachita nawe chipangano, ndipo ndidzakupatsa zidzukulu zambiri.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Ndipo Ine ndikulonjeza kuti ndidzakupatsa zidzukulu zambiri.” Onani mutuwo |