Hagai 2:5 - Buku Lopatulika5 monga momwe ndinapangana nanu muja munatuluka mu Ejipito, ndi Mzimu wanga unakhala pakati pa inu; musamaopa inu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 monga momwe ndinapangana nanu muja munatuluka m'Ejipito, ndi Mzimu wanga unakhala pakati pa inu; musamaopa inu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Musachite mantha, popeza kuti mzimu wanga uli pakati panu, monga momwe ndidalonjezera pamene munkatuluka ku Ejipito. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 ‘Izi ndi zimene ndinapangana nanu pamene munkatuluka ku Igupto. Ndipo Mzimu wanga uli pakati panu. Musachite mantha.’ Onani mutuwo |