Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 30:5 - Buku Lopatulika

Ndipo upange mphiko za mtengo wakasiya, ndi kuzikuta ndi golide.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo upange mphiko za mtengo wakasiya, ndi kuzikuta ndi golide.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mphiko zimenezi ikhale ya mtengo wa kasiya, ndipo uikute ndi golide.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Upange mizati yamtengo wa mkesha ndipo uyikute ndi golide.

Onani mutuwo



Eksodo 30:5
5 Mawu Ofanana  

Ndipo uzipanga mphiko za mtengo wakasiya, ndi kuzikuta ndi golide.


Mphetezo zikhale pafupi pa mitanda, zikhale zopisamo mphiko za kunyamulira nazo gome.


ndi zikopa za nkhosa zamphongo zonyika zofiira, ndi zikopa za akatumbu, ndi mtengo wakasiya;


Ndipo ulipangire mphete ziwiri zagolide pansi pa mkombero wake; uziike pa nthiti zake ziwiri, pa mbali zake ziwiri; zikhale zopisamo mphiko kulinyamula nazo.


Nuliike chakuno cha nsalu yotchinga ili ku likasa la mboni, patsogolo pa chotetezerapo chili pamwamba pa mboni, pomwe ndidzakomana ndi iwe.