Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 29:8 - Buku Lopatulika

Ndipo ubwere nao ana ake aamuna ndi kuwaveka malaya am'kati.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo ubwere nao ana ake amuna ndi kuwaveka malaya am'kati.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Kenaka ubwere ndi ana ake aamuna, ndipo uŵaveke miinjiro.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ubwere ndi ana ake aamuna ndipo uwavekenso minjiro

Onani mutuwo



Eksodo 29:8
4 Mawu Ofanana  

Ndipo upikule malaya am'kati abafuta a thonje losansitsa, nusoke nduwira wabafuta, nusokenso mpango wopikapika.


Ndipo usokere ana a Aroni malaya am'kati, nuwasokere mipango; uwasokerenso akapa akhale aulemerero ndi okoma.


Ndipo ubwere nao ana ake aamuna ndi kuwaveka malaya am'kati;


Ndipo Mose anatenga ana a Aroni, nawaveka malaya a m'kati, nawamanga m'chuuno ndi mipango, nawamanga akapa; monga Yehova adzauza Mose.