Eksodo 29:9 - Buku Lopatulika9 Uwamangirenso Aroni ndi ana ake aamuna mipango m'chuuno mwao, nuwamangire akapa pamutu pao; ndipo akhale ansembe mwa lemba losatha; nudzaze dzanja la Aroni ndi dzanja la ana ake aamuna. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Uwamangirenso Aroni ndi ana ake amuna mipango m'chuuno mwao, nuwamangire akapa pamutu pao; ndipo akhale ansembe mwa lemba losatha; nudzaze dzanja la Aroni ndi dzanja la ana ake amuna. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Uŵavekenso lamba m'chiwuno mwao ndi nduŵira. Motero iwoŵa adzakhala ansembe anga potsata lamulo langa losatha. Umu ndimo m'mene umdzozere Aroni ndi ana ake aamuna. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 ndi nduwira. Kenaka umange malamba Aaroniyo pamodzi ndi ana ake ndi kuwaveka nduwira. Motero unsembe udzakhala wawo malingana ndi lamulo ili losatha. “Umu ndi mmene udzadzozere Aaroni ndi ana ake aamuna. Onani mutuwo |