Eksodo 29:8 - Buku Lopatulika8 Ndipo ubwere nao ana ake aamuna ndi kuwaveka malaya am'kati. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Ndipo ubwere nao ana ake amuna ndi kuwaveka malaya am'kati. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Kenaka ubwere ndi ana ake aamuna, ndipo uŵaveke miinjiro. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Ubwere ndi ana ake aamuna ndipo uwavekenso minjiro Onani mutuwo |