Eksodo 28:40 - Buku Lopatulika40 Ndipo usokere ana a Aroni malaya am'kati, nuwasokere mipango; uwasokerenso akapa akhale aulemerero ndi okoma. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201440 Ndipo usokere ana a Aroni malaya am'kati, nuwasokere mipango; uwasokerenso akapa akhale aulemerero ndi okoma. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa40 “Ana a Aroni, uŵasokere miinjiro, malamba ndi nduŵira, kuti azisiyana ndi anthu ena, ndipo iwowo aziwoneka olemerera ndi olemekezeka. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero40 Upangirenso ana a Aaroni mwinjiro, malamba ndi nduwira kuti azioneka mwaulemu ndi molemekezeka. Onani mutuwo |