Eksodo 28:39 - Buku Lopatulika39 Ndipo upikule malaya am'kati abafuta a thonje losansitsa, nusoke nduwira wabafuta, nusokenso mpango wopikapika. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201439 Ndipo upikule malaya am'kati abafuta a thonje losansitsa, nusoke nduwira wabafuta, nusokenso mpango wopikapika. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa39 “Umsokerenso Aroni mwinjiro wa bafuta wokoma, ndipo umpangire nduŵira ya bafuta wokoma, ndiponso lamba wopetedwa mokongola. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero39 “Uluke mwinjiro wa nsalu yofewa yosalala ndiponso upange nduwira ya nsalu yofewa yosalala. Lamba wake akhale wolukidwa bwino ndi munthu waluso. Onani mutuwo |