Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 26:22 - Buku Lopatulika

Ndipo uzipanga matabwa asanu ndi limodzi kwa mbali ya chihema cha kumbuyo.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo uzipanga matabwa asanu ndi limodzi kwa mbali ya Kachisi ya kumbuyo.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Kumbuyo kwake kwa chihemacho, chakuzambwe, upange mafulemu asanu ndi limodzi.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Upange maferemu asanu ndi imodzi a kumbuyo kwa tenti, kumbali yakumadzulo.

Onani mutuwo



Eksodo 26:22
4 Mawu Ofanana  

Ndipo uzipangira chihema matabwa oimirika, a mtengo wakasiya.


makamwa awiri pansi pa thabwa limodzi, ndi makamwa awiri pansi pa thabwa lina.


Nupange matabwa awiri angodya za chihema cha kumbuyo.


Ndi ku mbali ya kumbuyo ya chihema kumadzulo anapanga matabwa asanu ndi limodzi.