Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 26:21 - Buku Lopatulika

21 makamwa awiri pansi pa thabwa limodzi, ndi makamwa awiri pansi pa thabwa lina.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

21 makamwa awiri pansi pa thabwa limodzi, ndi makamwa awiri pansi pa thabwa lina.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

21 ndi masinde makumi anai asiliva, aŵiri pa fulemu lililonse.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

21 Upangenso matsinde 40 asiliva, awiri pansi pa feremu iliyonse.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 26:21
3 Mawu Ofanana  

ndi pa mbali yake ina ya chihema, mbali ya kumpoto, pakhale matabwa makumi awiri; ndi makamwa asiliva makumi anai;


Ndipo uzipanga matabwa asanu ndi limodzi kwa mbali ya chihema cha kumbuyo.


Ndipo matalente zana limodzi a siliva ndiwo a kuyengera makamwa a malo opatulika, ndi makamwa a nsalu yotchinga; makamwa zana limodzi matalente zana limodzi, talente limodzi kamwa limodzi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa