Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Eksodo 26:21 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

21 Upangenso matsinde 40 asiliva, awiri pansi pa feremu iliyonse.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

21 makamwa awiri pansi pa thabwa limodzi, ndi makamwa awiri pansi pa thabwa lina.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

21 makamwa awiri pansi pa thabwa limodzi, ndi makamwa awiri pansi pa thabwa lina.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

21 ndi masinde makumi anai asiliva, aŵiri pa fulemu lililonse.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 26:21
3 Mawu Ofanana  

Ndipo mbali yakumpoto ya chihemacho upangenso maferemu makumi awiri.


Upange maferemu asanu ndi imodzi a kumbuyo kwa tenti, kumbali yakumadzulo.


Anagwiritsa ntchito siliva wolemera makilogalamu 3,400 kupanga matsinde 100 a ku malo wopatulika ndi makatani, ndipo makilogalamu 34 kupanga tsinde limodzi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa