Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 26:22 - Buku Lopatulika

22 Ndipo uzipanga matabwa asanu ndi limodzi kwa mbali ya chihema cha kumbuyo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

22 Ndipo uzipanga matabwa asanu ndi limodzi kwa mbali ya Kachisi ya kumbuyo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

22 Kumbuyo kwake kwa chihemacho, chakuzambwe, upange mafulemu asanu ndi limodzi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

22 Upange maferemu asanu ndi imodzi a kumbuyo kwa tenti, kumbali yakumadzulo.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 26:22
4 Mawu Ofanana  

Ndipo uzipangira chihema matabwa oimirika, a mtengo wakasiya.


makamwa awiri pansi pa thabwa limodzi, ndi makamwa awiri pansi pa thabwa lina.


Nupange matabwa awiri angodya za chihema cha kumbuyo.


Ndi ku mbali ya kumbuyo ya chihema kumadzulo anapanga matabwa asanu ndi limodzi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa