Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 26:20 - Buku Lopatulika

20 ndi pa mbali yake ina ya chihema, mbali ya kumpoto, pakhale matabwa makumi awiri; ndi makamwa asiliva makumi anai;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

20 ndi pa mbali yake ina ya Kachisi, mbali ya kumpoto, pakhale matabwa makumi awiri; ndi makamwa asiliva makumi anai;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

20 Ndipo kumpoto kwa chihemacho upangenso mafulemu makumi aŵiri,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

20 Ndipo mbali yakumpoto ya chihemacho upangenso maferemu makumi awiri.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 26:20
2 Mawu Ofanana  

Nuzipanga makamwa makumi anai asiliva pansi pa matabwa makumi awiri; makamwa awiri pansi pa thabwa limodzi kwa mitsukwa yake iwiri, ndi makamwa awiri pansi pa thabwa lina kwa mitsukwa yake iwiri;


makamwa awiri pansi pa thabwa limodzi, ndi makamwa awiri pansi pa thabwa lina.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa