Eksodo 36:27 - Buku Lopatulika27 Ndi ku mbali ya kumbuyo ya chihema kumadzulo anapanga matabwa asanu ndi limodzi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201427 Ndi ku mbali ya kumbuyo ya Kachisi kumadzulo anapanga matabwa asanu ndi limodzi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa27 Adapanganso mafulemu asanu ndi limodzi kumbuyo kwake kwa chihemacho chakuzambwe, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero27 Anapanganso maferemu asanu ndi imodzi a kumbuyo kwa tenti, kumbali yakumadzulo, Onani mutuwo |