Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 36:28 - Buku Lopatulika

28 Anapanganso matabwa awiri a kungodya za chihema, m'mbali zake ziwiri.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

28 Anapanganso matabwa awiri a kungodya za Kachisi, m'mbali zake ziwiri.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

28 ndiponso mafulemu aŵiri am'ngodya, kumbuyo kwake kwa chihemacho.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

28 ndiponso maferemu awiri a pa ngodya yakumbuyo kwenikweni kwa tenti.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 36:28
2 Mawu Ofanana  

Ndi ku mbali ya kumbuyo ya chihema kumadzulo anapanga matabwa asanu ndi limodzi.


Ndipo anaphatikizika pamodzi patsinde, naphatikizika pamodzi pamutu pake ndi mphete imodzi; anatero nao onse awiri pangodya ziwiri.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa