Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 25:6 - Buku Lopatulika

mafuta akuunikira, zonunkhira za mafuta odzoza, ndi za chofukiza cha fungo lokoma;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

mafuta akuunikira, zonunkhira za mafuta odzoza, ndi za chofukiza cha fungo lokoma;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

mafuta a nyale, zonunkhira za mafuta odzozera, ndiponso lubani wa fungo lokoma.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

mafuta anyale a olivi, zonunkhiritsa mafuta odzozera ndi zopangira lubani wonunkhira;

Onani mutuwo



Eksodo 25:6
7 Mawu Ofanana  

Ndipo uzipanga nyali zake, zisanu ndi ziwiri; ndipo ayatse nyali zake, ziwale pandunji pake.


ndi zikopa za nkhosa zamphongo zonyika zofiira, ndi zikopa za akatumbu, ndi mtengo wakasiya;


Ndipo uuze ana a Israele akutengere mafuta a azitona oyera opera akuunikira, kuti awalitse nyali kosalekeza.


Napanga mphiko za mtengo wakasiya, nazikuta ndi mkuwa.


Ndipo zoyang'anira Eleazara, mwana wa Aroni wansembe, ndizo mafuta a nyaliyo, ndi chofukiza cha fungo lokoma, ndi nsembe yaufa kosalekeza, ndi mafuta odzoza, udikiro wa chihema chonse, ndi zonse zili m'mwemo, malo opatulika, ndi zipangizo zake.