Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 38:6 - Buku Lopatulika

6 Napanga mphiko za mtengo wakasiya, nazikuta ndi mkuwa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 Napanga mphiko za mtengo wakasiya, nazikuta ndi mkuwa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 Adasema mphiko zonyamulira za mtengo wa kasiya, nazikuta ndi mkuŵa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 Anapanga nsichi zamtengo wa mkesha ndipo anazikuta ndi mkuwa.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 38:6
5 Mawu Ofanana  

ndi zikopa za nkhosa zamphongo zonyika zofiira, ndi zikopa za akatumbu, ndi mtengo wakasiya;


mafuta akuunikira, zonunkhira za mafuta odzoza, ndi za chofukiza cha fungo lokoma;


Ndipo anayengera mathungo anai a sefa wamkuwayo mphete zinai, zikhale zopisamo mphiko.


Ndipo anapisa mphikozo mu mphetezo pa mbali za guwa la nsembe, kulinyamulira nazo; analipanga ndi matabwa, lagweregwere.


Potero ndinapanga likasa la mtengo wakasiya, ndinasemanso magome awiri amiyala onga oyamba aja, ndi kukwera m'phirimo, magome awiri ali m'manja mwanga.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa