Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 38:5 - Buku Lopatulika

5 Ndipo anayengera mathungo anai a sefa wamkuwayo mphete zinai, zikhale zopisamo mphiko.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Ndipo anayengera mathungo anai a sefa wamkuwayo mphete zinai, zikhale zopisamo mphiko.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Adapanga mphete zinai ndipo adazilumikiza ku ngodya zinai za sefa ija, kuti apisemo mphiko zonyamulira.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Anapanga mphete zamkuwa zinayi ndipo anazilumikiza ku ngodya zinayi za sefa ija kuti zigwire nsichi zonyamulira.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 38:5
4 Mawu Ofanana  

Mphetezo zikhale pafupi pa mitanda, zikhale zopisamo mphiko za kunyamulira nazo gome.


Ndipo ulipangire sefa, malukidwe ake ndi amkuwa; nupange pa malukidwewo ngodya zake zinai mphete zinai zamkuwa.


Ndipo anapangira guwa la nsembelo sefa, malukidwe ake nja mkuwa, pansi pa khoma lamkati lake wakulekeza pakati pake.


Napanga mphiko za mtengo wakasiya, nazikuta ndi mkuwa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa