Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 12:10 - Buku Lopatulika

Ndipo musasiyako kufikira m'mawa; koma yotsalira kufikira m'mamawayo muipsereze ndi moto.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo musasiyako kufikira m'mawa; koma yotsalira kufikira m'mamawayo muipsereze ndi moto.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Musasiyeko nyama ina mpaka m'maŵa, motero ina ikatsalako, muitenthe.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Musadzasiye nyama ina mpaka mmawa, ngati ina idzatsala mpaka mmawa, mudzayitenthe.

Onani mutuwo



Eksodo 12:10
9 Mawu Ofanana  

Ndipo Mose ananena nao, Palibe munthu asiyeko kufikira m'mawa.


Usapereka mwazi wa nsembe yanga pamodzi ndi mkate wa chotupitsa; ndi mafuta a madyerero anga asagonamo kufikira m'mawa.


Ndipo ikatsalako nyama yodzaza manja, kapena mkate kufikira m'mawa, pamenepo utenthe zotsalazo ndi moto; asazidye popeza nchopatulika ichi.


Usapereke mwazi wa nsembe yanga yophera pamodzi ndi mkate wachotupitsa; ndi nsembe yophera ya chikondwerero cha Paska asaisiye kufikira m'mawa.


Tsiku lomwelo mwaipha, ndi m'mawa mwake muidye; ngati katsalirako kanthu tsiku lachitatu, muzikatentha ndi moto.


Idyedwe tsiku lomwelo; musamasiyako kufikira m'mawa; Ine ndine Yehova.


Asasiyeko kufikira m'mawa, kapena kuthyolapo fupa; auchite monga mwa lemba lonse la Paska.