Eksodo 12:10 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Musadzasiye nyama ina mpaka mmawa, ngati ina idzatsala mpaka mmawa, mudzayitenthe. Onani mutuwoBuku Lopatulika10 Ndipo musasiyako kufikira m'mawa; koma yotsalira kufikira m'mamawayo muipsereze ndi moto. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ndipo musasiyako kufikira m'mawa; koma yotsalira kufikira m'mamawayo muipsereze ndi moto. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Musasiyeko nyama ina mpaka m'maŵa, motero ina ikatsalako, muitenthe. Onani mutuwo |