Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Levitiko 19:6 - Buku Lopatulika

6 Tsiku lomwelo mwaipha, ndi m'mawa mwake muidye; ngati katsalirako kanthu tsiku lachitatu, muzikatentha ndi moto.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 Tsiku lomwelo mwaipha, ndi m'mawa mwake muidye; ngati katsalirako kanthu tsiku lachitatu, muzikatentha ndi moto.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 Muidye tsiku lomwe mwaiperekalo, kapena m'maŵa mwake, koma zotsalako mpaka pa tsiku lachitatu muzitenthe.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 Nsembe izidyedwa tsiku lomwe mwayiperekalo kapena mmawa mwake. Chilichonse chotsala mpaka tsiku lachitatu chiyenera kutenthedwa.

Onani mutuwo Koperani




Levitiko 19:6
4 Mawu Ofanana  

Ndipo musasiyako kufikira m'mawa; koma yotsalira kufikira m'mamawayo muipsereze ndi moto.


Ndipo pamene muphera Yehova nsembe yoyamika, muiphere kuti mulandiridwe.


Akakadya konse tsiku lachitatu kali chonyansa, kosavomerezeka:


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa