Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 16:19 - Buku Lopatulika

19 Ndipo Mose ananena nao, Palibe munthu asiyeko kufikira m'mawa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

19 Ndipo Mose ananena nao, Palibe munthu asiyeko kufikira m'mawa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

19 Pamenepo Mose adaŵauza kuti, “Munthu aliyense asasungeko mpaka m'maŵa.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

19 Ndipo Mose anawawuza kuti, “Wina aliyense asasunge mpaka mmawa.”

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 16:19
5 Mawu Ofanana  

Ndipo musasiyako kufikira m'mawa; koma yotsalira kufikira m'mamawayo muipsereze ndi moto.


Koma sanammvere Mose; ndipo ena anasiyako kufikira m'mawa; koma unagwa mphutsi, nununkha. Ndipo Mose anakwiya nao.


Ndipo ananena nao, Ichi ndi chomwe Yehova analankhula, Mawa ndiko kupuma, Sabata lopatulika la Yehova; chimene muziotcha, otchani, ndi chimene muziphika phikani; ndi chotsala chikukhalireni chosungika kufikira m'mawa.


Usapereka mwazi wa nsembe yanga pamodzi ndi mkate wa chotupitsa; ndi mafuta a madyerero anga asagonamo kufikira m'mawa.


Chifukwa chake musadere nkhawa za mawa; pakuti mawa adzadzidera nkhawa iwo okha. Zikwanire tsiku zovuta zake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa