Eksodo 16:19 - Buku Lopatulika19 Ndipo Mose ananena nao, Palibe munthu asiyeko kufikira m'mawa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Ndipo Mose ananena nao, Palibe munthu asiyeko kufikira m'mawa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Pamenepo Mose adaŵauza kuti, “Munthu aliyense asasungeko mpaka m'maŵa.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Ndipo Mose anawawuza kuti, “Wina aliyense asasunge mpaka mmawa.” Onani mutuwo |